Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 148:11 - Buku Lopatulika

Mafumu a padziko ndi mitundu yonse ya anthu; zinduna ndi oweruza onse a padziko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mafumu a padziko ndi mitundu yonse ya anthu; zinduna ndi oweruza onse a padziko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu mafumu a pa dziko lapansi ndi anthu a mitundu yonse, inu akuluakulu ndi olamulira dziko lapansi!

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu mafumu a dziko lapansi ndi anthu a mitundu yonse, inu akalonga ndi olamulira a dziko lapansi.

Onani mutuwo



Masalimo 148:11
12 Mawu Ofanana  

Pamenepo amitundu adzaopa dzina la Yehova, ndi mafumu onse a dziko lapansi ulemerero wanu.


Amitundu onse mudawalenga adzadza nadzagwada pamaso panu, Ambuye; nadzalemekeza dzina lanu.


Ndipo mafumu adzakulera, ndi akazi ao aakulu adzakuyamwitsa; iwo adzakugwadira ndi nkhope zao zoyang'ana pansi, nadzaseteka fumbi la m'mapazi ako: ndipo iwe udzadziwa kuti Ine ndine Yehova, ndi iwo amene alindira Ine sadzakhala ndi manyazi.


Ndipo amitundu adzafika kwa kuunika kwako, ndi mafumu kwa kuyera kwa kutuluka kwako.


Ndipo amitundu adzayendayenda mwa kuunika kwake; ndi mafumu a dziko atenga ulemerero wao kulowa nao momwemo.