Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 147:7 - Buku Lopatulika

Yamikani Yehova ndi kuthira mang'ombe; muimbireni Mulungu wathu zomlemekeza pazeze:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yamikani Yehova ndi kuthira mang'ombe; muimbireni Mulungu wathu zomlemekeza pazeze:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Imbirani Chauta mothokoza, imbirani Mulungu wathu nyimbo yokoma ndi pangwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Imbirani Yehova ndi mayamiko; imbani nyimbo kwa Mulungu ndi pangwe.

Onani mutuwo



Masalimo 147:7
8 Mawu Ofanana  

Imbirani Mulungu, maufumu a dziko lapansi inu; imbirani Ambuye zomlemekeza.


Muimbireni Yehova zomlemekeza ndi zeze; ndi zeze ndi mau a salimo.