Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 147:4 - Buku Lopatulika

Awerenga nyenyezi momwe zili; azitcha maina zonsezi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Awerenga nyenyezi momwe zili; azitcha maina zonsezi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amadziŵa chiŵerengero cha nyenyezi, zonse amazitcha maina ake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amadziwa chiwerengero cha nyenyezi, ndipo iliyonse amayitchula dzina.

Onani mutuwo



Masalimo 147:4
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anamtulutsa iye kunja, nati, Tayang'anatu kumwamba, uwerenge nyenyezi, ngati ukhoza kuziwerenga zimenezo: ndipo anati kwa iye, Zoterezo zidzakhala mbeu zako.


Mlemekezeni, dzuwa ndi mwezi; mlemekezeni, nyenyezi zonse zounikira.


Pakuona ine thambo la kumwamba lanu, ntchito ya zala zanu, mwezi ndi nyenyezi, zimene munazikhazika,


Kwezani maso anu kumwamba, muone amene analenga izo, amene atulutsa khamu lao ndi kuziwerenga; azitcha zonse maina ao, ndi mphamvu zake zazikulu, ndi popeza ali wolimba mphamvu, palibe imodzi isoweka.