Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 144:3 - Buku Lopatulika

Yehova, munthu ndani kuti mumdziwa? Mwana wa munthu kuti mumsamalira?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yehova, munthu ndani kuti mumdziwa? Mwana wa munthu kuti mumsamalira?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Chauta, kodi munthu nchiyani, kuti muzimsamala? Mwana wa munthu nchiyani, kuti muzimganizira?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu Yehova, munthu nʼchiyani kuti mumamusamalira, mwana wa munthu kuti muzimuganizira?

Onani mutuwo



Masalimo 144:3
7 Mawu Ofanana  

Munthu nchiyani kuti akhale woyera, wobadwa ndi mkazi kuti akhale wolungama?


Munthu ndani kuti mumkuze, ndi kuti muike mtima wanu pa iye,


munthu ndani kuti mumkumbukira? Ndi mwana wa munthu kuti mucheza naye?


Pakuti munamchepsa pang'ono ndi Mulungu, munamveka iye korona wa ulemerero ndi ulemu.


Siyani munthu, amene mpweya wake uli m'mphuno mwake; chifukwa m'mene awerengedwamo ndi muti?


Koma wina anachita umboni pena, nati, Munthu nchiyani kuti mumkumbukira iye? Kapena mwana wa munthu kuti mucheza naye?