Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 140:1 - Buku Lopatulika

Ndilanditseni, Yehova, kwa munthu woipa; ndisungeni kwa munthu wachiwawa;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndilanditseni, Yehova, kwa munthu woipa; ndisungeni kwa munthu wachiwawa;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pulumutseni, Inu Chauta, kwa anthu oipa. Tchinjirizeni kwa anthu ankhanza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Landitseni Yehova kwa anthu oyipa; tetezeni kwa anthu ankhanza,

Onani mutuwo



Masalimo 140:1
8 Mawu Ofanana  

Munthu wamlomo sadzakhazikika padziko lapansi; choipa chidzamsaka munthu wachiwawa kuti chimgwetse.


Ndilindireni Yehova, ndisalowe m'manja mwa woipa; ndisungeni kwa munthu wachiwawa; kwa iwo akuti akankhe mapazi anga.


Ukani Yehova, Mumtsekereze, mumgwetse, landitsani moyo wanga kwa woipa ndi lupanga lanu;


Andipulumutsa kwa adani anga. Inde mundikweza pa iwo akundiukira ine, mundikwatula kwa munthu wachiwawa.


Mundiweruzire, Mulungu, ndipo mundinenere mlandu kwa anthu opanda chifundo. Mundilanditse kwa munthu wonyenga ndi wosalungama.


Ndilanditseni, Mulungu wanga, m'dzanja la woipa, m'dzanja la munthu wosalungama ndi wachiwawa.