Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 139:6 - Buku Lopatulika

Kudziwa ichi kundiposa ndi kundidabwitsa: Kundikhalira patali, sindifikirako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kudziwa ichi kundilaka ndi kundidabwitsa: Kundikhalira patali, sindifikirako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nzeru zimenezi nzopitirira nzeru zanga, nzapamwamba, sindingathe kuzimvetsa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nzeru zimenezi ndi zopitirira nzeru zanga, ndi zapamwamba kuti ine ndizipeze.

Onani mutuwo



Masalimo 139:6
8 Mawu Ofanana  

Taonani, awa ndi malekezero a njira zake; ndi chimene tikumva za Iye ndi chinong'onezo chaching'ono; koma kugunda kwa mphamvu yake akuzindikiritsa ndani?


Ndani uyu abisa uphungu wosadziwa kanthu? Chifukwa chake ndinafotokozera zimene sindinazizindikire, zondidabwitsa, zosazidziwa ine.


Mudzandiiwala chiiwalire, Yehova, kufikira liti? Mudzandibisira ine nkhope yanu kufikira liti?


Inu, Yehova, Mulungu wanga, zodabwitsa zanu mudazichita nzambiri, ndipo zolingirira zanu za pa ife; palibe wina wozifotokozera Inu; ndikazisimba ndi kuzitchula, zindichulukira kuziwerenga.


Zinthu zitatu zindithetsa nzeru, ngakhale zinai, sindizidziwa:


Ha! Kuya kwake kwa kulemera ndi kwa nzeru ndi kwa kudziwa kwake kwa Mulungu! Osasanthulikadi maweruzo ake, ndi njira zake nzosalondoleka!