Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 139:5 - Buku Lopatulika

Munandizinga kumbuyo ndi kumaso, nimunaika dzanja lanu pa ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Munandizinga kumbuyo ndi kumaso, nimunaika dzanja lanu pa ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mumandizinga kumbuyo ndi kutsogolo, ndipo mumandisanjika dzanja lanu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mumandizinga kumbuyo ndi kutsogolo komwe; mwasanjika dzanja lanu pa ine.

Onani mutuwo



Masalimo 139:5
6 Mawu Ofanana  

Palibe wakutiweruza, wakutisanjika ife tonse awiri manja ake.


Mngelo wa Yehova azinga kuwatchinjiriza iwo akuopa Iye, nawalanditsa iwo.


Koma sanatulutse dzanja lake pa akulu a ena a Israele; ndipo anapenya Mulungu, nadya, namwa.


Mulungu wamuyaya ndiye mokhaliramo mwako; ndi pansipo pali manja osatha. Ndipo aingitsa mdani pamaso pako, nati, Ononga.


Ndipo pamene ndinamuona Iye, ndinagwa pa mapazi ake ngati wakufa; ndipo anaika dzanja lake lamanja pa ine, nati, Usaope, Ine ndine Woyamba ndi Wotsiriza,