Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 139:22 - Buku Lopatulika

Ndidana nao ndi udani weniweni, ndiwayesa adani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndidana nao ndi udani weniweni, ndiwayesa adani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndimadana nawo ndi chidani chenicheni. Ndimaŵayesa adani anga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndimadana nawo kwathunthu; ndi adani anga.

Onani mutuwo



Masalimo 139:22
2 Mawu Ofanana  

Munthu akadza kwa Ine, wosada atate wake ndi amake, ndi mkazi wake, ndi ana, ndi abale, ndi alongo ake, inde ndi moyo wake womwe wa iye mwini, sangathe kukhala wophunzira wanga.