Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 137:2 - Buku Lopatulika

Pa msondodzi uli m'mwemo tinapachika mazeze athu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pa msondodzi uli m'mwemo tinapachika mazeze athu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kumeneko tidapachika apangwe athu pa mitengo ya misondodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kumeneko, pa mitengo ya misondozi tinapachika apangwe athu,

Onani mutuwo



Masalimo 137:2
6 Mawu Ofanana  

Yamikani Yehova ndi zeze; muimbireni ndi chisakasa cha zingwe khumi.


Utsani salimo, bwera nakoni kalingaka, zeze wokondwetsa pamodzi ndi chisakasa.


Kusangalala kwa mangaka kwalekeka, phokoso la iwo amene asekera litha, kukondwa kwa mngoli kwalekeka.


Ndipo ndidzaleketsa phokoso la nyimbo zako, ndi kulira kwa mazeze ako sikudzamvekanso.


Ndipo ndidzasanduliza zikondwerero zanu zikhale maliro, ndi nyimbo zanu zikhale za maliro, ndi kufikitsa ziguduli m'chuuno monse, ndi mpala pamutu uliwonse; nadzakhala ngati maliro a mwana mmodzi yekha, ndi chitsiriziro chake ngati tsiku lowawa.


Ndipo mau a anthu oimba zeze, ndi a oimba, ndi a oliza zitoliro, ndi a oomba malipenga sadzamvekanso konse mwa iwe; ndipo mmisiri aliyense wa machitidwe ali onse sadzapezedwanso konse mwa iwe; ndi mau a mphero sadzamvekanso konse mwa iwe;