Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 135:20 - Buku Lopatulika

A nyumba ya Levi inu, lemekezani Yehova: Inu akuopa Yehova, lemekezani Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

A nyumba ya Levi inu, lemekezani Yehova: Inu akuopa Yehova, lemekezani Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu a banja la Levi, tamandani Chauta! Inu amene mumaopa Chauta, tamandani Chauta!

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu nyumba ya Levi, tamandani Yehova; Inu amene mumaopa Iye, tamandani Yehova.

Onani mutuwo



Masalimo 135:20
3 Mawu Ofanana  

Aleluya; Lemekezani, inu atumiki a Yehova; lemekezani dzina la Yehova.


Israele, khulupirira Yehova: Ndiye mthandizi wao ndi chikopa chao.


Ndipo Paulo ananyamuka, nakodola ndi dzanja, nati, Amuna a Israele, ndi inu akuopa Mulungu, mverani.