A nyumba ya Levi inu, lemekezani Yehova: Inu akuopa Yehova, lemekezani Yehova.
Inu a banja la Levi, tamandani Chauta! Inu amene mumaopa Chauta, tamandani Chauta!
Inu nyumba ya Levi, tamandani Yehova; Inu amene mumaopa Iye, tamandani Yehova.
Aleluya; Lemekezani, inu atumiki a Yehova; lemekezani dzina la Yehova.
Israele, khulupirira Yehova: Ndiye mthandizi wao ndi chikopa chao.
Ndipo Paulo ananyamuka, nakodola ndi dzanja, nati, Amuna a Israele, ndi inu akuopa Mulungu, mverani.