Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 135:15 - Buku Lopatulika

Mafano a amitundu ndiwo siliva ndi golide, ntchito ya manja a anthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mafano a amitundu ndiwo siliva ndi golide, ntchito ya manja a anthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mafano a mitundu ina ya anthu ndi asiliva ndi agolide chabe, ndi opangidwa ndi manja a anthu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mafano a mitundu ya anthu ndi siliva ndi golide, opangidwa ndi manja a anthu.

Onani mutuwo



Masalimo 135:15
9 Mawu Ofanana  

Ndipo anaponya milungu yao pamoto; pakuti iyo sinali milungu, koma ntchito yopangidwa ndi manja a anthu, mtengo ndi mwala; chifukwa chake iwo anaiononga.


Popeza tsono tili mbadwa za Mulungu, sitiyenera kulingalira kuti umulungu uli wofanafana ndi golide, kapena siliva, kapena mwala, wolocha ndi luso ndi zolingalira za anthu.


Ndipo kumeneko mudzatumikira milungu, ntchito ya manja a anthu, mtengo ndi mwala, yosapenya, kapena kumva, kapena kudya, kapena kununkhiza.