Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 132:7 - Buku Lopatulika

Tidzalowa mokhalamo Iye; tidzagwadira kumpando wa mapazi ake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tidzalowa mokhalamo Iye; tidzagwadira kumpando wa mapazi ake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Tiyeni tipite kumalo kumene Chauta amakhala. Tiyeni tikapembedze ku mpando wake wachifumu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Tiyeni tipite ku malo ake okhalamo; tiyeni tikamulambire pa mapazi ake.

Onani mutuwo



Masalimo 132:7
9 Mawu Ofanana  

Nditsegulireni zipata za chilungamo; ndidzalowamo, ndidzayamika Yehova.


Ndinakondwera m'mene ananena nane, Tiyeni kunyumba ya Yehova.


Koma ine, mwa kuchuluka kwa chifundo chanu ndidzalowa m'nyumba yanu; ndidzagwada kuyang'ana Kachisi wanu woyera ndi kuopa Inu.


Tiyeni, tipembedze tiwerame; tigwade pamaso pa Yehova, amene anatilenga.


Mkwezeni Yehova Mulungu wathu, ndipo gwadirani poponderapo mapazi ake: Iye ndiye Woyera.


Mkwezeni Yehova Mulungu wathu, ndipo gwadirani paphiri lake loyera; pakuti Yehova Mulungu wathu ndiye woyera.


Ndipo anthu ambiri adzanka, nati, Tiyeni tikwere kunka kuphiri la Yehova, kunyumba ya Mulungu wa Yakobo; ndipo Iye adzatiphunzitsa za njira zake, ndipo tidzayenda m'mayendedwe ake; chifukwa mu Ziyoni mudzatuluka chilamulo, ndi mau a Yehova kuchokera mu Yerusalemu.


Ambuye waphimbatu ndi mtambo mwana wamkazi wa Ziyoni, pomkwiyira! Wagwetsa pansi kuchokera kumwamba kukoma kwake kwa Israele; osakumbukira poponda mapazi ake tsiku la mkwiyo wake.