Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 132:4 - Buku Lopatulika

ngati ndidzalola maso anga agone, kapena zikope zanga ziodzere;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ngati ndidzalola maso anga agone, kapena zikope zanga ziodzere;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

sindidzalola kuti ndikhale m'tulo kapena kuti zikope zanga ziwodzere,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

sindidzalola kuti maso anga agone, kapena zikope zanga ziwodzere,

Onani mutuwo



Masalimo 132:4
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anaika chakudya pamaso pake: koma anati, Sindidzadya ndisananene chimene ndadzera. Ndipo anati, Nenatu.


Usaone tulo m'maso mwako, ngakhale kuodzera zikope zako.


Ndipo anati, Khala ulipo, mwana wanga, mpaka udziwa umo ukhalire mlandu; pakuti munthuyo sadzauleka mpaka atautha mlanduwo lero lino.