Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 131:3 - Buku Lopatulika

Israele, uyembekezere Yehova, kuyambira tsopano kufikira kosatha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Israele, uyembekezere Yehova, kuyambira tsopano kufikira kosatha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iwe Israele, khulupirira Chauta kuyambira tsopano mpaka muyaya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.

Onani mutuwo



Masalimo 131:3
7 Mawu Ofanana  

Koma ife tidzalemekeza Yehova kuyambira tsopano kufikira nthawi yonse. Aleluya.


Yehova adzasungira kutuluka kwako ndi kulowa kwako, kuyambira tsopano kufikira nthawi zonse.


Israele, uyembekezere Yehova; chifukwa kwa Yehova kuli chifundo, kwaonso kuchulukira chiombolo.


Wodala munthu amene akhala naye Mulungu wa Yakobo kuti amthandize, chiyembekezo chake chili pa Yehova, Mulungu wake.


Khulupirirani Yehova nthawi zamuyaya, pakuti mwa Ambuye Yehova muli thanthwe lachikhalire.