Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 130:8 - Buku Lopatulika

Ndipo adzaombola Israele ku mphulupulu zake zonse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo adzaombola Israele ku mphulupulu zake zonse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adzaombola Israele ku machimo ake onse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye mwini adzawombola Israeli ku machimo ake onse.

Onani mutuwo



Masalimo 130:8
8 Mawu Ofanana  

Ine ndafafaniza monga mtambo wochindikira zolakwa zako, ndi monga mtambo machimo ako; bwerera kwa Ine, pakuti ndakuombola.


Ndipo ndidzawayeretsa kuchotsa mphulupulu yao, imene anandichimwira Ine; ndipo ndidzakhululukira mphulupulu zao zimene anandichimwira, nandilakwira Ine.


Ndipo adzabala mwana wamwamuna, ndipo udzamutcha dzina lake Yesu; pakuti Iyeyo adzapulumutsa anthu ake kumachimo ao.


Wolemekezeka Ambuye, Mulungu wa Israele; chifukwa Iye anayang'ana, nachitira anthu ake chiombolo.


Pakuti uchimo sudzachita ufumu pa inu; popeza simuli a lamulo koma a chisomo.


amene anadzipereka yekha m'malo mwa ife, kuti akatiombole ife kuzoipa zonse, nakadziyeretsere yekha anthu akhale ake enieni, achangu pa ntchito zokoma.