Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 129:3 - Buku Lopatulika

Olima analima pamsana panga; anatalikitsa mipere yao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Olima analima pamsana panga; anatalikitsa mipere yao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Pondikwapula adani anga adachita ngati kulima pamsana panga, kulima mizere yaitali.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu otipula analima pa msana panga ndipo anapangapo mizere yayitali:

Onani mutuwo



Masalimo 129:3
4 Mawu Ofanana  

Kodi ukhoza kumanga njati ndi lamba lake ilime m'mchera? Kapena idzakutsata kodi kufafaniza nthumbira m'zigwa?


Mafupa athu amwazika pakamwa pa manda, monga ngati akumba nanyimphula nthaka yapansi.


Ndinapereka msana wanga kwa omenya, ndi masaya anga kwa iwo amene anakudzula tsitsi langa; sindinabisire nkhope yanga manyazi ndi kulavulidwa.


Ndidzachiika m'dzanja la iwo amene avutitsa iwe; amene anena kumoyo wako, Gwada pansi kuti ife tipite; ndipo iwe wagonetsa pamsana pako monga pansi, ndi monga khwalala kwa iwo amene apita pamenepo.