Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 124:5 - Buku Lopatulika

madzi odzikuza akadapita pa moyo wathu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

madzi odzikuza akadapita pa moyo wathu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

bwenzi madzi amphamvu atatimiza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

madzi a mkokomo akanatikokolola.

Onani mutuwo



Masalimo 124:5
3 Mawu Ofanana  

ndi kuti, Ufike mpaka apa, osapitirirapo; apa adzaletseka mafunde ako odzikuza?


Kodi simundiopa Ine? Ati Yehova: simudzanthunthumira pamaso pa Ine, amene ndinaika mchenga chilekaniro cha nyanja, ndi lemba lamuyaya kuti isapitirirepo? Ndipo ngakhale mafunde ake achita gavigavi, alephera; ngakhale akokoma, sangathe kupitirirapo.