Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 124:2 - Buku Lopatulika

Akadapanda kukhala nafe Yehova, pakutiukira anthu:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Akadapanda kukhala nafe Yehova, pakutiukira anthu:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta akadapanda kukhala pa mbali yathu, pamene anthu adatiwukira,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

akanapanda kukhala mbali yathu Yehova, potiwukira anthuwo,

Onani mutuwo



Masalimo 124:2
8 Mawu Ofanana  

Pakuti andizinga agalu, msonkhano wa oipa wanditsekereza; andiboola m'manja anga ndi m'mapazi anga.


Yehova! Ha! Achuluka nanga akundisautsa ine! Akundiukira ine ndi ambiri.


Ambiri amati kwa moyo wanga, alibe chipulumutso mwa Mulungu.


Woipa aunguza wolungama, nafuna kumupha.


Mwa Mulungu ndidzalemekeza mau ake, mwa Yehova ndidzalemekeza mau ake.