Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 122:2 - Buku Lopatulika

Mapazi athu alinkuima m'zipata zanu, Yerusalemu

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mapazi athu alinkuima m'zipata zanu, Yerusalemu

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mapazi athu akhala akuima m'kati mwa zipata zako, iwe Yerusalemu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.

Onani mutuwo



Masalimo 122:2
5 Mawu Ofanana  

Koma ndinasankha Yerusalemu, kuti dzina langa likhale komweko; ndinasankhanso Davide akhale mfumu ya anthu anga Israele.


Lowani kuzipata zake ndi chiyamiko, ndi kumabwalo ake ndi chilemekezo: Myamikeni; lilemekezeni dzina lake.


Apita mwamphamvu naonjezapo mphamvu, aoneka pamaso pa Mulungu mu Ziyoni.


Undiumbire guwa la nsembe ladothi, nundiphere pomwepo nsembe zako zopsereza, ndi nsembe zako zamtendere, nkhosa zako ndi ng'ombe zako; paliponse ndikumbukiritsa anthu dzina langa ndidzakudzera ndi kukudalitsa.