Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 121:6 - Buku Lopatulika

Dzuwa silidzawamba usana, mwezi sudzakupanda usiku.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Dzuwa silidzawamba usana, mwezi sudzakupanda usiku.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Dzuŵa silidzakupweteka masana, mwezi sudzakuvuta usiku.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana, kapena mwezi nthawi ya usiku.

Onani mutuwo



Masalimo 121:6
4 Mawu Ofanana  

Iwo sadzakhala ndi njala, pena ludzu; ngakhale thukuta, pena dzuwa silidzawatentha; pakuti Iye amene wawachitira chifundo, adzawatsogolera, ngakhale pa akasupe a madzi adzawatsogolera.


Ndipo kunali, potuluka dzuwa Mulungu anaika mphepo ya kum'mawa yotentha, ndipo dzuwa linatentha mutu wake wa Yona, nalefuka iye, nadzipempherera kuti afe; nati, Kundikomera ine kufa, kukhala ndi moyo ai.


sadzamvanso njala, kapena ludzu, kapena silidzawatentha dzuwa, kapena chitungu chilichonse;