Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 121:1 - Buku Lopatulika

Ndikweza maso anga kumapiri: Thandizo langa lidzera kuti?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndikweza maso anga kumapiri: Thandizo langa lidzera kuti?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndimakweza maso anga ku mapiri. Kodi chithandizo changa chimachokera kuti?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndikweza maso anga ku mapiri; kodi thandizo langa limachokera kuti?

Onani mutuwo



Masalimo 121:1
8 Mawu Ofanana  

Ndinafuulira kwa Yehova mu msauko wanga, ndipo anandivomereza.


Ndikweza maso anga kwa Inu, kwa Inu wakukhala kumwamba.


Koma Ine ndadzoza mfumu yanga Pa Ziyoni, phiri langa loyera.


koma anasankha fuko la Yuda, Phiri la Ziyoni limene analikonda.


Maziko ake ali m'mapiri oyera.


Ndipo anthu ambiri adzanka, nati, Tiyeni tikwere kunka kuphiri la Yehova, kunyumba ya Mulungu wa Yakobo; ndipo Iye adzatiphunzitsa za njira zake, ndipo tidzayenda m'mayendedwe ake; chifukwa mu Ziyoni mudzatuluka chilamulo, ndi mau a Yehova kuchokera mu Yerusalemu.


Ndithu akhulupirira mwachabe chithandizo cha kuzitunda, ndi phokoso la kumapiri; ndithu mwa Yehova Mulungu wathu muli chipulumutso cha Israele.