Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 120:7 - Buku Lopatulika

Ine ndikuti, Mtendere; koma polankhula ine, iwowa akuti, Nkhondo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ine ndikuti, Mtendere; koma polankhula ine, iwowa akuti, Nkhondo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ine ndimafuna mtendere, koma ndikalankhula za mtendere, iwo amafuna nkhondo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.

Onani mutuwo



Masalimo 120:7
12 Mawu Ofanana  

Ine ndine wa awo amene ali amtendere ndi okhulupirika mu Israele; inu mulikufuna kuononga mzinda ndi mai wa mu Israele; mudzamezeranji cholowa cha Yehova?


M'malo mwa chikondi changa andibwezera udani; koma ine, kupemphera ndiko.


Futuka pazoipa, nuchite zabwino, funa mtendere ndi kuulondola.


Pakuti salankhula zamtendere, koma apangira chiwembu odekha m'dziko.


Anatulutsa manja ake awagwire iwo akuyanjana naye, anaipsa pangano lake.


Odala ali akuchita mtendere; chifukwa adzatchedwa ana a Mulungu.


Ngati nkutheka, monga momwe mukhoza, khalani ndi mtendere ndi anthu onse.


Londolani mtendere ndi anthu onse, ndi chiyeretso chimene, akapanda ichi, palibe mmodzi adzaona Ambuye:


Ndipo Yefita anatumanso mithenga kwa mfumu ya ana a Amoni;