Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 120:3 - Buku Lopatulika

Adzakuninkhanji, adzakuonjezeranji, lilime lonyenga iwe?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Adzakuninkhanji, adzakuonjezeranji, lilime lonyenga iwe?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mulungu adzakuchitani chiyani, anthu onyenganu? Kodi adzakupatsani chilango cha mtundu wanji?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?

Onani mutuwo



Masalimo 120:3
3 Mawu Ofanana  

Pakuti chiyembekezo cha wonyoza Mulungu nchiyani pomlikhatu Mulungu, pomchotsera moyo wake?


Pakuti munthu adzapindulanji, akalandira dziko lonse, nataya moyo wake? Kapena munthu adzaperekanji chosintha ndi moyo wake?


Ndipo munali nazo zobala zanji nthawi ija, m'zinthu zimene muchita nazo manyazi tsopano? Pakuti chimaliziro cha zinthu izi chili imfa.