Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 118:25 - Buku Lopatulika

Tikupemphani, Yehova, tipulumutseni tsopano; tikupemphani, Yehova, tipindulitseni tsopano.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tikupemphani, Yehova, tipulumutseni tsopano; tikupemphani, Yehova, tipindulitseni tsopano.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tipulumutseni, tikukupemphani Inu Chauta. Chauta, tikukupemphani kuti zinthu zitiyendere bwino.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu Yehova, tipulumutseni; Yehova, tipambanitseni.

Onani mutuwo



Masalimo 118:25
5 Mawu Ofanana  

Yehova, pulumutsani, mfumuyo ativomereze tsiku lakuitana ife.


ndipulumutseni m'kamwa mwa mkango; inde mwandiyankha ine ndili pa nyanga za njati.


Ndipulumutseni Mulungu; pakuti madzi afikira moyo wanga.


Koma ine, pemphero langa lili kwa Inu, Yehova, m'nyengo yolandirika; Mulungu, mwa chifundo chanu chachikulu, mundivomereze ndi choonadi cha chipulumutso chanu.


Ndipo chisomo chake cha Ambuye Mulungu wathu chikhalire pa ife; ndipo mutikhazikitsire ife ntchito ya manja athu; inde, ntchito ya manja athu muikhazikitse.