Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 118:23 - Buku Lopatulika

Ichi chidzera kwa Yehova; nchodabwitsa ichi pamaso pathu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ichi chidzera kwa Yehova; nchodabwitsa ichi pamaso pathu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta ndiye amene wachita zimenezi, zimenezi nzodabwitsa pamaso pathu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova ndiye wachita zimenezi ndipo nʼzodabwitsa pamaso pathu.

Onani mutuwo



Masalimo 118:23
8 Mawu Ofanana  

amene achita zazikulu ndi zosalondoleka, zinthu zodabwitsa zosawerengeka.


Ichinso chifumira kwa Yehova wa makamu, uphungu wake uzizwitsa ndi nzeru yake impambana.


Taonani, opeputsa inu, zizwani, kanganukani; kuti ndigwiritsa ntchito Ine masiku anu, ntchito imene simudzaikhulupirira wina akakuuzani.


Koma pakuona kulimbika mtima kwa Petro ndi Yohane, ndipo pozindikira kuti ndiwo anthu osaphunzira ndi opulukira, anazizwa ndipo anawazindikira, kuti adakhala pamodzi ndi Yesu.