Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 118:21 - Buku Lopatulika

Ndidzakuyamikani, popeza munandiyankha, ndipo munakhala chipulumutso changa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndidzakuyamikani, popeza munandiyankha, ndipo munakhala chipulumutso changa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndikukuyamikani popeza kuti mwandiyankha, ndipo mwasanduka Mpulumutsi wanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndidzakuyamikani chifukwa Inu munandiyankha; mwakhala chipulumutso changa.

Onani mutuwo



Masalimo 118:21
7 Mawu Ofanana  

Ndimkonda, popeza Yehova amamva mau anga ndi kupemba kwanga.


Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga; ndipo anakhala chipulumutso changa.


Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga, ndipo wakhala chipulumutso changa; ameneyo ndiye Mulungu wanga, ndidzamlemekeza; ndiye Mulungu wa kholo langa, ndidzamveketsa.


Taonani, Mulungu ndiye chipulumutso changa; ndidzakhulupirira, sindidzaopa; pakuti Yehova Mwini ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga, Iye ndiye chipulumutso changa.


Atero Yehova, Nthawi yondikomera ndakuyankha Iwe, ndi tsiku la chipulumutso ndakuthandiza; ndipo ndidzakusunga ndi kupatsa Iwe ukhale pangano la anthu, kuti ukhazikitse dziko, nuwalowetse m'zolowa zopasuka m'malo abwinja;