Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 118:19 - Buku Lopatulika

Nditsegulireni zipata za chilungamo; ndidzalowamo, ndidzayamika Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nditsegulireni zipata za chilungamo; ndidzalowamo, ndidzayamika Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsekulireni zipata za Nyumba ya Mulungu, kuti ndifike ku malo ake achilungamo, ndikathokoze Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsekulireni zipata zachilungamo, kuti ndifike kudzayamika Yehova.

Onani mutuwo



Masalimo 118:19
10 Mawu Ofanana  

Lowani kuzipata zake ndi chiyamiko, ndi kumabwalo ake ndi chilemekezo: Myamikeni; lilemekezeni dzina lake.


Mulungu, mokhala mwake moyera, ndiye Atate wa ana amasiye, ndi woweruza wa akazi amasiye.


Tidze nacho chiyamiko pamaso pake, timfuulire Iye mokondwera ndi nyimbo.


Tsegulani pazipata, kuti mtundu wolungama, umene uchita zoonadi, ulowemo.


Yehova ndiye wondipulumutsa ine; Chifukwa chake tidzaimba nyimbo zanga, ndi zoimba zazingwe Masiku onse a moyo wathu m'nyumba ya Yehova.


Hezekiya anatinso, Chizindikiro nchiyani, kuti ndidzakwera kunka kunyumba ya Yehova?


Odala iwo amene atsuka miinjiro yao, kuti akakhale nao ulamuliro pa mtengo wa moyo, ndi kuti akalowe m'mzinda pazipata.