Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 118:16 - Buku Lopatulika

Dzanja lamanja la Yehova likwezeka, Dzanja lamanja la Yehova lichita mwamphamvu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Dzanja lamanja la Yehova likwezeka, Dzanja lamanja la Yehova lichita mwamphamvu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

dzanja lamanja la Chauta lapambana, dzanja lamanja la Chauta limagonjetsa mwamphamvu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Dzanja lamanja la Yehova latukulidwa mmwamba Dzanja lamanja la Yehova lachita zamphamvu!”

Onani mutuwo



Masalimo 118:16
2 Mawu Ofanana  

Dzanja lanu lamanja, Yehova, lalemekezedwa ndi mphamvu, dzanja lanu lamanja, Yehova, laphwanya mdani.