Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 115:9 - Buku Lopatulika

Israele, khulupirira Yehova: Ndiye mthandizi wao ndi chikopa chao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Israele, khulupirira Yehova: Ndiye mthandizi wao ndi chikopa chao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iwe Israele, khulupirira Chauta. Chauta ndiye mthandizi wako ndi chishango chako.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu Aisraeli, dalirani Yehova; Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.

Onani mutuwo



Masalimo 115:9
15 Mawu Ofanana  

Iwo akukhulupirira Yehova akunga phiri la Ziyoni, losasunthika, likhazikika kosatha.


Israele, uyembekezere Yehova; chifukwa kwa Yehova kuli chifundo, kwaonso kuchulukira chiombolo.


Khulupirira Yehova, ndipo chita chokoma; khala m'dziko, ndipo tsata choonadi.


Khulupirirani pa Iye nyengo zonse, anthu inu, tsanulirani mitima yanu pamaso pake. Mulungu ndiye pothawirapo ife.


Pakuti Yehova Mulungu ndiye dzuwa ndi chikopa; Yehova adzapatsa chifundo ndi ulemerero; sadzakaniza chokoma iwo akuyenda angwiro.


Ndipo tsopano, ngati mudzamvera mau anga ndithu, ndi kusunga chipangano changa, ndidzakuyesani chuma changa cha padera koposa mitundu yonse ya anthu; pakuti dziko lonse lapansi ndi langa;


Mau onse a Mulungu ali oyengeka; ndiye chikopa cha iwo amene amkhulupirira.


Ndiwo chabe, ndiwo chiphamaso; pa nthawi ya kulangidwa kwao adzatha.


kuti ife amene tinakhulupirira Khristu kale tikayamikitse ulemerero wake.


Wodala iwe, Israele; akunga iwe ndani, mtundu wa anthu opulumutsidwa ndi Yehova, ndiye chikopa cha thandizo lako, Iye amene akhala lupanga la ukulu wako! Ndi adani ako adzakugonjera; ndipo udzaponda pa misanje yao.