Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 113:8 - Buku Lopatulika

Kuti amkhalitse pamodzi ndi akulu, pamodzi ndi akulu a anthu ake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kuti amkhalitse pamodzi ndi akulu, pamodzi ndi akulu a anthu ake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amaŵakhazika pamodzi ndi mafumu, mafumu a anthu a Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

amawakhazika pamodzi ndi mafumu, pamodzi ndi mafumu a anthu ake.

Onani mutuwo



Masalimo 113:8
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Farao anati kwa Yosefe, Taona, ndakhazika iwe wolamulira dziko lonse la Ejipito.


Sawachotsera wolungama maso ake, koma pamodzi ndi mafumu pa mpando wao awakhazika chikhazikire, ndipo akwezeka.


M'malo mwa makolo ako mudzakhala ana ako, udzawaika akhale mafumu m'dziko lonse lapansi.


Pogona inu m'makola a zoweta, mukhala ngati mapiko a njiwa okulira ndi siliva, ndi nthenga zake zokulira ndi golide woyenga wonyezimira.


Amuutsa waumphawi m'fumbi, nanyamula wosowa padzala, kukamkhalitsa kwa akalonga; ndi kuti akhale nacho cholowa cha chimpando cha ulemerero. Chifukwa nsanamira za dziko lapansi nza Yehova, ndipo Iye anakhazika dziko pa izo.