Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 113:1 - Buku Lopatulika

Aleluya; Lemekezani, inu atumiki a Yehova; lemekezani dzina la Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Aleluya; Lemekezani, inu atumiki a Yehova; lemekezani dzina la Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tamandani Chauta! Mtamandeni, inu atumiki ake, tamandani dzina la Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tamandani Yehova. Mutamandeni, inu atumiki a Yehova, tamandani dzina la Yehova.

Onani mutuwo



Masalimo 113:1
11 Mawu Ofanana  

Aleluya. Wodala munthu wakuopa Yehova, wakukondwera kwambiri ndi malamulo ake.


Taonani, lemekezani Yehova, atumiki a Yehova inu nonse, akuimirira m'nyumba ya Yehova usiku.


A nyumba ya Levi inu, lemekezani Yehova: Inu akuopa Yehova, lemekezani Yehova.


Ntchito zanu zonse zidzakuyamikani, Yehova; ndi okondedwa anu adzakulemekezani.


Yehova aombola moyo wa anyamata ake, ndipo sadzawatsutsa kumlandu onse akukhulupirira Iye.


Ndipo mbumba ya atumiki ake idzalilandira; ndipo iwo akukonda dzina lake adzakhala m'mwemo.


Ndipo mau anachokera kumpando wachifumu, ndi kunena, Lemekezani Mulungu wathu akapolo ake onse akumuopa Iye, aang'ono ndi aakulu.