Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 109:9 - Buku Lopatulika

Ana ake akhale amasiye, ndi mkazi wake wamasiye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ana ake akhale amasiye, ndi mkazi wake wamasiye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ana ake akhale amasiye, ndipo mkazi wake akhale mfedwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ana ake akhale amasiye ndipo mkazi wake akhale wopanda mwamuna.

Onani mutuwo



Masalimo 109:9
3 Mawu Ofanana  

ndi mkwiyo wanga udzayaka, ndipo ndidzapha inu ndi lupanga; ndipo akazi anu adzakhala amasiye, ndi ana anu omwe.


Chifukwa chake mupereke ana ao kunjala, mupereke iwo kumphamvu ya lupanga; akazi ao akhale opanda ana, ndi amasiye; amuna ao aphedwe ndi imfa, ndi anyamata ao apandidwe ndi lupanga kunkhondo.


Ndife amasiye opanda atate, amai athu akunga akazi amasiye.