Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 109:8 - Buku Lopatulika

Masiku ake akhale owerengeka; wina alandire udindo wake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Masiku ake akhale owerengeka; wina alandire udindo wake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Masiku ake akhale oŵerengeka, wina alandire udindo wake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masiku ake akhale owerengeka; munthu wina atenge malo ake a utsogoleri.

Onani mutuwo



Masalimo 109:8
3 Mawu Ofanana  

Koma Inu, Mulungu, mudzawatsitsira kudzenje la chionongeko. Anthu okhetsa mwazi ndi achinyengo masiku ao sadzafikira nusu; koma ine ndidzakhulupirira Inu.


Ndipo iye anataya pansi ndalamazo pa Kachisi, nachokapo, nadzipachika yekha pakhosi.