Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 109:11 - Buku Lopatulika

Wokongoletsa agwire zonse ali nazo; ndi alendo alande za ntchito yake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wokongoletsa agwire zonse ali nazo; ndi alendo alande za ntchito yake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Wokongoza ndalama amlande zonse zimene ali nazo. Alendo afunkhe zimene adapindula ndi ntchito yake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Wokongoza alande zonse zimene ali nazo; alendo afunkhe ntchito za manja ake.

Onani mutuwo



Masalimo 109:11
7 Mawu Ofanana  

Chimene adagwiriracho ntchito, adzachibweza, osachimeza; sadzakondwera monga mwa zolemera zake adaziona.


Zokolola zao anjala azidya, azitenga ngakhale kuminga, ndi aludzu ameza chuma chao.


ndipo mudzafufuza usana, monga wakhungu amafufuza mumdima, ndipo simudzapindula nazo njira zanu; koma mudzakhala wopsinjika, nadzakuberani masiku onse, wopanda wina wakukupulumutsani.