Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 108:2 - Buku Lopatulika

Galamukani, chisakasa ndi zeze; ndidzauka ndekha mamawa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Galamukani, chisakasa ndi zeze; ndidzauka ndekha mamawa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu zeze ndi pangwe, tiyeni lirani. Ndidzadzutsa dzuŵa ndi nyimbo zanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Dzukani, zeze ndi pangwe! Ine ndidzadzutsa mʼbandakucha.

Onani mutuwo



Masalimo 108:2
7 Mawu Ofanana  

Lemekezani Yehova, inu, ntchito zake zonse, ponseponse pali ufumu wake: Lemekeza Yehova, moyo wanga iwe.


Yamikani Yehova ndi zeze; muimbireni ndi chisakasa cha zingwe khumi.


Galamuka, ulemu wanga; galamukani chisakasa ndi zeze! Ndidzauka ndekha mamawa.


Ndidzalemekeza dzina la Mulungu ndi kuliimbira, ndipo ndidzambukitsa ndi kumyamika.


Utsani salimo, bwera nakoni kalingaka, zeze wokondwetsa pamodzi ndi chisakasa.


Galamuka, Debora, galamuka, galamuka, galamuka, unene nyimbo; uka, Baraki, manga nsinga ndende zako, mwana wa Abinowamu, iwe.