Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 108:12 - Buku Lopatulika

Tithandizeni mumsauko; pakuti chipulumutso cha munthu ndi chabe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tithandizeni mumsauko; pakuti chipulumutso cha munthu ndi chabe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tithandizeni kulimbana ndi adani athuwo, pakuti chithandizo cha munthu nchopandapake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tithandizeni ife kulimbana ndi mdani, pakuti thandizo la munthu ndi lopanda pake.

Onani mutuwo



Masalimo 108:12
9 Mawu Ofanana  

Ndamva zambiri zotere; inu nonse ndinu otonthoza mtima mondilemetsa.


Mulungu sadzabweza mkwiyo wake; athandizi odzikuza awerama pansi pa Iye.


Siyani munthu, amene mpweya wake uli m'mphuno mwake; chifukwa m'mene awerengedwamo ndi muti?


Koma Aejipito ndiwo anthu, si Mulungu; ndi akavalo ao ali nyama, si mzimu; ndipo pamene Yehova adzatambasula dzanja lake, wothandiza adzaphunthwa, ndi wothandizidwa adzagwa, ndipo iwo onse awiri pamodzi adzalephera.


Maso athu athedwa, tikali ndi moyo, poyembekeza thandizo chabe; kudikira tinadikira mtundu wosatha kupulumutsa.