Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 104:9 - Buku Lopatulika

Munaika malire kuti asapitirireko; kuti asabwererenso kuphimba dziko lapansi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Munaika malire kuti asapitirireko; kuti asabwererenso kuphimba dziko lapansi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Madziwo Inu mudaŵaikira malire oti asabzole, kuti asaphimbenso dziko lapansi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu munayika malire ndipo sangathe kudutsa, iwo sadzamizanso dziko lapansi.

Onani mutuwo



Masalimo 104:9
6 Mawu Ofanana  

Analembera madziwo malire, mpaka polekeza kuunika ndi mdima.


Amaunjika madzi a m'nyanja monga mulu, amakundika zakudya mosungiramo.


Pakuti kumeneku kuli kwa Ine monga madzi a Nowa; pakuti monga ndinalumbira kuti madzi a Nowa sadzamizanso padziko lapansi, momwemo ndinalumbira kuti sindidzakukwiyira iwe, pena kukudzudzula.


Kodi simundiopa Ine? Ati Yehova: simudzanthunthumira pamaso pa Ine, amene ndinaika mchenga chilekaniro cha nyanja, ndi lemba lamuyaya kuti isapitirirepo? Ndipo ngakhale mafunde ake achita gavigavi, alephera; ngakhale akokoma, sangathe kupitirirapo.