Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 104:8 - Buku Lopatulika

anakwera m'mapiri, anatsikira m'zigwa, kufikira malo mudawakonzeratu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

anakwera m'mapiri, anatsikira m'zigwa, kufikira malo mudawakonzeratu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mapiri adatumphuka, zigwa zidatsika, mpaka kumene Inu mudaakonzeratu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu munamiza mapiri, iwo anatsikira ku zigwa kumalo kumene munawakonzera.

Onani mutuwo



Masalimo 104:8
3 Mawu Ofanana  

Ndipo madzi analinkuchepa kufikira mwezi wakhumi; mwezi wakhumi tsiku loyamba mwezi ndipo padaoneka mitu ya mapiri.


Amaunjika madzi a m'nyanja monga mulu, amakundika zakudya mosungiramo.


Mapiri asanakhazikike, zitunda zisanapangidwe, ndinabadwa.