Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 104:7 - Buku Lopatulika

Pa kudzudzula kwanu anathawa; anathawa msanga liu la bingu lanu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pa kudzudzula kwanu anathawa; anathawa msanga liu la bingu lanu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mutaŵadzudzula, madziwo adathaŵa, atamva mkokomo wa bingu lanu, adamwazika.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma pakudzudzula kwanu madzi anathawa, pa mkokomo wa bingu lanu iwo anamwazika;

Onani mutuwo



Masalimo 104:7
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Mulungu anakumbukira Nowa ndi zamoyo zonse, ndi nyama zonse zimene zinali pamodzi naye m'chingalawamo; ndipo Mulungu anapititsa mphepo padziko lapansi, naphwa madzi;


Ndipo anadzudzula Nyanja Yofiira, ndipo inaphwa: Potero anawayendetsa mozama ngati m'chipululu.


Ndipo zidaoneka zoyendamo madzi, nafukuka maziko a dziko lapansi, mwa kudzudzula kwanu, Yehova, mwa mpumo wa mpweya wa m'mphuno mwanu.


Liu la bingu lanu linatengezanatengezana; mphezi zinaunikira ponse pali anthu; dziko lapansi linanjenjemera ndi kugwedezeka.


polimbitsa Iye thambo la kumwamba, pokula akasupe a zozama.


Ndipo anauka, nadzudzula mphepo, nati kwa nyanja, kuti, Tonthola, khala bata. Ndipo mphepo inaleka, ndipo kunagwa bata lalikulu.