Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 104:16 - Buku Lopatulika

Mitengo ya Yehova yadzala ndi madzi; mikungudza ya ku Lebanoni imene anaioka;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mitengo ya Yehova yadzala ndi madzi; mikungudza ya ku Lebanoni imene anaioka;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mitengo ya Chauta amaithirira ndi madzi ambiri, mikungudza ya ku Lebanoni imene adaibzala.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mitengo ya Yehova ndi yothiriridwa bwino, mikungudza ya ku Lebanoni imene Iye anadzala.

Onani mutuwo



Masalimo 104:16
4 Mawu Ofanana  

Liu la Yehova lithyola mitengo yamkungudza; inde Yehova athyola mikungudza ya ku Lebanoni.


Kuonetsera chifundo chanu mamawa, ndi chikhulupiriko chanu usiku uliwonse.


paphiri lothuvuka la Israele ndidzaioka, ndipo idzaphuka nthambi ndi kubala zipatso, nidzakhala mkungudza wokoma, ndi m'munsi mwake mudzakhala mbalame zilizonse za mapiko aliwonse; mu mthunzi wa nthambi zake zidzabindikira.


Ziyalika monga zigwa, monga minda m'mphepete mwa nyanja, monga khonje wooka Yehova, monga mikungudza m'mphepete mwa madzi.