Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 104:10 - Buku Lopatulika

Atumiza akasupe alowe m'makwawa; ayenda pakati pa mapiri:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Atumiza akasupe alowe m'makwawa; ayenda pakati pa mapiri:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu mumatumphutsa akasupe m'zigwa, mitsinje imayenda pakati pa mapiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye achititsa akasupe kutulutsa madzi kupita ku zigwa; madziwo amayenda pakati pa mapiri.

Onani mutuwo



Masalimo 104:10
4 Mawu Ofanana  

Asanduliza chipululu chikhale thawale, ndi dziko louma likhale akasupe a madzi.


Ndipo mchenga wong'azimira udzasanduka thamanda, ndi nthaka yopanda madzi idzasanduka zitsime zamadzi; m'malo a ankhandwe m'mene iwo anagona, mudzakhala udzu ndi mabango ndi milulu.


Ndidzagwetsa mitsinje pazitunda zoti see, ndi akasupe pakati pa zigwa; ndidzasandutsa chipululu, chikhale thamanda lamadzi, ndi mtunda wouma ukhale magwero a madzi.


Pakuti Yehova Mulungu wanu akulowetsani m'dziko lokoma, dziko la mitsinje yamadzi, la akasupe ndi la maiwe akutuluka m'zigwa, ndi m'mapiri;