Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 103:16 - Buku Lopatulika

Pakuti mphepo ikapitapo pakhala palibe: Ndi malo ake salidziwanso.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti mphepo ikapitapo pakhala palibe: Ndi malo ake salidziwanso.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma mphepo ikaombapo, duŵalo pamakhala palibe, siliwonekanso pa malo ake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

koma mphepo imawombapo ndipo silionekanso ndipo malo ake sakumbukirikanso.

Onani mutuwo



Masalimo 103:16
8 Mawu Ofanana  

ndipo Enoki anayendabe ndi Mulungu; ndipo panalibe iye; pakuti Mulungu anamtenga.


Koma munthu akufa atachita liondeonde inde, munthu apereka mzimu wake, ndipo ali kuti?


Diso lidamuonalo silidzamuonanso; ndi malo ake sadzampenyanso.


Mau a wina ati, Fuula. Ndipo ndinati, Kodi ndifuule chiyani? Anthu onse ndi udzu, ndi kukoma kwao konse kunga duwa la m'thengo;


udzu unyala, duwa lifota; chifukwa mpweya wa Yehova waombapo; zoonadi anthu ndi udzu.