Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 103:10 - Buku Lopatulika

Sanatichitira monga mwa zolakwa zathu, kapena kutibwezera monga mwa mphulupulu zathu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Sanatichitira monga mwa zolakwa zathu, kapena kutibwezera monga mwa mphulupulu zathu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Satilanga moyenerera machimo athu, satibwezera molingana ndi zolakwa zathu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

satichitira molingana ndi machimo athu, kapena kutibwezera molingana ndi mphulupulu zathu.

Onani mutuwo



Masalimo 103:10
8 Mawu Ofanana  

Ndipo zitatigwera zonsezi chifukwa cha ntchito zathu zoipa ndi kupalamula kwathu kwakukulu; popeza inu Mulungu wathu mwatilanga motichepsera mphulupulu zathu, ndi kutipatsa chipulumutso chotere;


Ndipo mwa nsoni zanu zochuluka simunawathe, kapena kuwataya; popeza Inu ndinu Mulungu wa chisomo ndi chifundo.


nakufotokozere zinsinsi za nzeru, popeza zipindikapindika machitidwe ao! Chifukwa chake dziwa kuti Mulungu akuiwalira mphulupulu zina.


Apenyerera anthu, ndi kuti, ndinachimwa, ndaipsa choongokacho, ndipo sindinapindule nako.


Mukasunga mphulupulu, Yehova, adzakhala chilili ndani, Ambuye?


Chifukwa chakusathedwa ife ndicho chifundo cha Yehova, pakuti chisoni chake sichileka,


Yehova, ndinamva mbiri yanu ndi mantha; Yehova, tsitsimutsani ntchito yanu pakati pa zaka, pakati pa zaka mudziwitse; pa mkwiyo mukumbukire chifundo.