Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 102:27 - Buku Lopatulika

Koma Inu ndinu yemweyo, ndi zaka zanu sizifikira kutha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Inu ndinu yemweyo, ndi zaka zanu sizifikira kutha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Inu simusintha, zaka zanu sizitha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Inu simusintha, ndipo zaka zanu sizidzatha.

Onani mutuwo



Masalimo 102:27
8 Mawu Ofanana  

Taonani, Mulungu ndiye wamkulu, ndipo sitimdziwa; chiwerengo cha zaka zake nchosasanthulika.


Pakuti pamaso panu zaka zikwi zikhala ngati dzulo, litapita, ndi monga ulonda wa usiku.


Pakuti Ine Yehova sindisinthika, chifukwa chake inu ana a Yakobo simunathedwe.


Yesu anati kwa iwo, Indetu, indetu, ndinena kwa inu, asanayambe kukhala Abrahamu ndipo Ine ndilipo.


Yesu Khristu ali yemweyo dzulo, ndi lero, ndi kunthawi zonse.


Mphatso iliyonse yabwino, ndi chininkho chilichonse changwiro zichokera Kumwamba, zotsika kwa Atate wa mauniko, amene alibe chisanduliko, kapena mthunzi wa chitembenukiro.


Ine ndine Alefa ndi Omega, ati Ambuye Mulungu, amene ali, amene adali, ndi amene alinkudza, Wamphamvuyonse.