Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 102:23 - Buku Lopatulika

Iye analanda mphamvu yanga panjira; anachepsa masiku anga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Iye analanda mphamvu yanga panjira; anachepsa masiku anga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta wathyola mphamvu zanga ndisanakule, wafupikitsa masiku anga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anathyola mphamvu zanga pa nthawi ya moyo wanga; Iyeyo anafupikitsa masiku anga.

Onani mutuwo



Masalimo 102:23
10 Mawu Ofanana  

Pakuti chomsamalitsa nyumba yake nchiyani, atapita iye, chiwerengo cha miyezi yake chitadulidwa pakati?


Ndipo padzakhala masiku otsiriza, kuti phiri la nyumba ya Yehova lidzakhazikika pansonga ya mapiri, ndipo lidzakwezedwa pamwamba pa zitunda; mitundu yonse idzasonkhana kumeneko.


Ndipo anthu ambiri adzanka, nati, Tiyeni tikwere kunka kuphiri la Yehova, kunyumba ya Mulungu wa Yakobo; ndipo Iye adzatiphunzitsa za njira zake, ndipo tidzayenda m'mayendedwe ake; chifukwa mu Ziyoni mudzatuluka chilamulo, ndi mau a Yehova kuchokera mu Yerusalemu.


Pa nthawi yomweyo adzatcha Yerusalemu mpando wa Yehova; ndipo mitundu yonse idzasonkhanidwa kumeneko, ku dzina la Yehova, ku Yerusalemu; ndipo sadzayendanso konse m'kuumirira kwa mtima wao woipa.