Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 102:22 - Buku Lopatulika

Posonkhana pamodzi mitundu ya anthu, ndi maufumu kuti atumikire Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Posonkhana pamodzi mitundu ya anthu, ndi maufumu kuti atumikire Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

pamene mitundu ya anthu ndi mafumu adzasonkhana kuti apembedze Chauta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

pamene mitundu ya anthu ndi maufumu adzasonkhana kuti alambire Yehova.

Onani mutuwo



Masalimo 102:22
11 Mawu Ofanana  

Ndodo yachifumu siidzachoka mwa Yuda, kapena wolamulira pakati pa mapazi ake, kufikira atadza Silo; ndipo anthu adzamvera iye.


Malekezero onse a dziko lapansi adzakumbukira nadzatembenukira kwa Yehova, ndipo mafuko onse a amitundu adzagwadira pamaso panu.


Mau a alonda ako! Akweza mau, aimba pamodzi; pakuti adzaona maso ndi maso, pamene Yehova abwerera kudza ku Ziyoni.


Kondwani zolimba, imbani pamodzi, inu malo abwinja a pa Yerusalemu; pakuti Yehova watonthoza mtima wa anthu ake, waombola Yerusalemu.


Ndipo Uthenga uwu Wabwino wa Ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi, ukhale mboni kwa anthu a mitundu yonse; ndipo pomwepo chidzafika chimaliziro.


mu mphamvu ya zizindikiro ndi zozizwitsa, mu mphamvu ya Mzimu Woyera; kotero kuti ine kuyambira ku Yerusalemu ndi kuzungulirako kufikira ku Iliriko, ndinakwanitsa Uthenga Wabwino wa Khristu;