Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 9:6 - Buku Lopatulika

Pakuti sanadziwe chimene adzayankha; chifukwa anachita mantha ndithu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti sanadziwe chimene adzayankha; chifukwa anachita mantha ndithu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ankatero chifukwa chosoŵa chonena, pakuti iye ndi anzake aja anali atagwidwa ndi mantha aakulu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

(Iye sanadziwe choti anene, anali ndi mantha akulu).

Onani mutuwo



Marko 9:6
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Petro anayankha, nanena ndi Yesu, Rabi, kutikomera ife kukhala pano; ndipo timange misasa itatu; umodzi wa inu, ndi wina wa Mose, ndi wina wa Eliya.


Ndipo panadza mtambo wakuwaphimba iwo; ndipo mau munatuluka m'mtambomo, kuti, Uyu ndiye Mwana wanga wokondedwa; mverani Iye.


Ndipo panali polekana iwo aja ndi Iye, Petro anati kwa Yesu, Ambuye, nkwabwino kuti tili pano; ndipo timange misasa itatu, umodzi wa Inu, ndi wina wa Mose, ndi wina wa Eliya; wosadziwa iye chimene alikunena.


Ndipo pamene ndinamuona Iye, ndinagwa pa mapazi ake ngati wakufa; ndipo anaika dzanja lake lamanja pa ine, nati, Usaope, Ine ndine Woyamba ndi Wotsiriza,