Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 9:16 - Buku Lopatulika

Ndipo anawafunsa iwo, Mufunsana nao chiyani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anawafunsa iwo, Mufunsana nao chiyani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iye adaŵafunsa kuti, “Kodi mukutsutsana zotani?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anafunsa kuti, “Mukukangana nawo chiyani iwowa?”

Onani mutuwo



Marko 9:16
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Afarisi anatuluka, nayamba kufunsana naye, ndi kufuna kwa Iye chizindikiro chochokera Kumwamba, namuyesa Iye.


Ndipo pomwepo anthu onse a khamulo, pakumuona Iye, anazizwa kwambiri, namthamangira Iye, namlonjera.


Ndipo wina wa m'khamulo anamyankha Iye, kuti, Mphunzitsi, ndadza naye kwa Inu mwana wanga, ali nao mzimu wosalankhula;