Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 8:8 - Buku Lopatulika

Ndipo anadya nakhuta; ndipo anatola makombo madengu asanu ndi awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anadya nakhuta; ndipo anatola makombo madengu asanu ndi awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu adadya mpaka kukhuta. Adatola zotsala, nadzaza madengu asanu ndi aŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu anadya ndipo anakhuta. Atamaliza, ophunzira anatola buledi ndi nsomba zotsalira ndi kudzaza madengu asanu ndi awiri.

Onani mutuwo



Marko 8:8
16 Mawu Ofanana  

Muolowetsa dzanja lanu, nimukwaniritsira zamoyo zonse chokhumba chao.


Ndipo anadya onse, nakhuta; ndipo anatola makombo otsala, nadzala madengu khumi ndi iwiri.


Ndipo onsewa anadya, nakhuta: ndipo anatola makombo otsala madengu asanu ndi awiri odzala.


Penanso mikate isanu ndi iwiri ija ya anthu zikwi zinai, ndi madengu angati munawatola?


Ndipo iwo anali ngati zikwi zinai; ndipo Iye analawirana nao.


Anawakhutitsa anjala ndi zinthu zabwino, ndipo eni chuma anawachotsa opanda kanthu.


Gwirani ntchito si chifukwa cha chakudya chimene chitayika koma cha chakudya chimene chitsalira kumoyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani inu; pakuti ameneyo Atate, ndiye Mulungu, adamlembera chizindikiro.