Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 8:16 - Buku Lopatulika

Ndipo anatsutsana wina ndi mnzake, nanena kuti, Tilibe mikate.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anatsutsana wina ndi mnzake, nanena kuti, Tilibe mikate.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo ophunzirawo adayamba kukambirana nkumati, “Akuterotu chifukwa tilibe buledi.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anakambirana wina ndi mnzake ndipo anati, “Ndi chifukwa choti tilibe buledi.”

Onani mutuwo



Marko 8:16
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anawalamula, nanena, Yang'anirani, penyani kuti mupewe chotupitsa mkate cha Afarisi, ndi chotupitsa mkate cha Herode.


Ndipo Yesu pamene anazindikira, ananena nao, Bwanji mutsutsana chifukwa mulibe mkate? Kodi kufikira tsopano simuzindikira, nisimudziwitsa? Kodi muli nayo mitima yanu youma?


Ndipo anatsutsana mwa okha, nanena, Ngati tinena uchokera Kumwamba; adzati, Simunamkhulupirire chifukwa ninji?


Ndipo anayamba kutsutsana kuti wamkulu mwa iwo ndani.